Course Content
Kufunika kwa Zisudzo
Chisudzo ndi nkhani yochitika kapena yopeka yomwe imafotokoza zinthu mokhala ngati zikuchitika kumene.
0/2
MITU YONSE MNKHANIYI
0/1
Khoswe Wa Padenga
Kukamba za Bonzo, Goli, Khoswe, Anne ndi Jubeki
0/2
Mudzi Wa Mfumu Tandwe
Kuonongeka kwa zachilengedwe ndi mavuto ena
0/3
CHAMDOTHE NDI ZISUDZO ZINA

Gwero lachisudzo  

Mchira wabuluzi womwe udapezeka m’chipanda chamowa womwe Nadzonzi adatenga kwa  Nasiwelo ndipo adampatsa mamuna wake Ndileya  

Ochita chisudzo  

  1. Ndileya: Mwamuna wa Nadzonzi 
  2. Nadzonzi : Mkazi wa Ndileya 
  3. Chidazi: Malume a Nadzonzi 
  4. Nachuma: Mchemwali wamkulu wa Nadzonzi 
  5. Amfumu  
  6. Anthu  

Malo mwachidule  

Kunyumba kwa Ndileya ndi Nadzonzi  

Kuchitsime 

Kunyumba kwa Nasiwelo  

Ku Zomba (kuchipatala cha anthu amisala)  

Kunyumba kwa a Chidazi  

Ku bwalo lamilandu (kwa amfumu)

error: Content is protected !!
Scroll to Top